Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:61 - Buku Lopatulika

Koma Nadabu ndi Abihu adafa, muja anabwera nao moto wachilendo pamaso pa Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Nadabu ndi Abihu adafa, muja anabwera nao moto wachilendo pamaso pa Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Nadabu ndi Abihu adafa chifukwa adaapereka moto wosaloledwa pamaso pa Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Nadabu ndi Abihu anafa pamene anapereka nsembe pamaso pa Yehova ndi moto wachilendo).

Onani mutuwo



Numeri 26:61
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Aroni anadzitengera Eliseba, mwana wamkazi wa Aminadabu, mlongo wake wa Nasoni, akhale mkazi wake; ndipo anambalira Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara.


Koma Nadabu ndi Abihu anafa pamaso pa Yehova muja anabwera nao moto wachilendo pamaso pa Yehova, m'chipululu cha Sinai, ndipo analibe ana; koma Eleazara ndi Itamara anachita ntchito ya nsembe pamaso pa atate wao Aroni.