Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:60 - Buku Lopatulika

60 Ndipo Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara anabadwira Aroni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

60 Ndipo Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara anabadwira Aroni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

60 Aroni adabala Nadabu, Abihu, Eleazara ndi Itamara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

60 Aaroni anali abambo a Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:60
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Aroni anadzitengera Eliseba, mwana wamkazi wa Aminadabu, mlongo wake wa Nasoni, akhale mkazi wake; ndipo anambalira Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara.


Ndipo maina ao a ana aamuna a Aroni ndi awa: Woyamba Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara.


Ndipo asunge zipangizo zonse za chihema chokomanako, ndi udikiro wa ana a Israele, kuichita ntchito ya Kachisi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa