Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:60 - Buku Lopatulika

Ndipo Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara anabadwira Aroni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara anabadwira Aroni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Aroni adabala Nadabu, Abihu, Eleazara ndi Itamara.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aaroni anali abambo a Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara.

Onani mutuwo



Numeri 26:60
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Aroni anadzitengera Eliseba, mwana wamkazi wa Aminadabu, mlongo wake wa Nasoni, akhale mkazi wake; ndipo anambalira Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara.


Ndipo maina ao a ana aamuna a Aroni ndi awa: Woyamba Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara.


Ndipo asunge zipangizo zonse za chihema chokomanako, ndi udikiro wa ana a Israele, kuichita ntchito ya Kachisi.