Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:19 - Buku Lopatulika

Ana aamuna a Yuda, ndiwo Eri ndi Onani; ndipo Eri ndi Onani anamwalira m'dziko la Kanani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ana amuna a Yuda, ndiwo Eri ndi Onani; ndipo Eri ndi Onani anamwalira m'dziko la Kanani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana aamuna a Yuda anali Ere ndi Onani, koma iwowo adafera m'dziko la Kanani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Eri ndi Onani anali ana aamuna a Yuda, koma anafera mu Kanaani.

Onani mutuwo



Numeri 26:19
5 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana aamuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli.


Ana a Yuda: Perezi, Hezironi, ndi Karimi, ndi Huri, ndi Sobala.


A ana a Yuda, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;