Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:16 - Buku Lopatulika

Ozini, ndiye kholo la banja la Aozini; Eri, ndiye kholo la banja la Aeri;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ozini, ndiye kholo la banja la Aozini; Eri, ndiye kholo la banja la Aeri;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ozini anali kholo la banja la Aozini. Eri anali kholo la banja la Aeri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuchokera mwa Ozini, fuko la Aozini; kuchokera mwa Eri, fuko la Aeri;

Onani mutuwo



Numeri 26:16
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Gadi: Zifiyoni, ndi Hagi, ndi Suni, ndi Eziboni, ndi Eri, ndi Arodi, ndi Areli.


Ana aamuna a Gadi monga mwa mabanja ao ndiwo: Zefoni, ndiye kholo la banja la Azefoni; Hagi, ndiye kholo la banja la Ahagi; Suni, ndiye kholo la banja la Suni;


Arodi, ndiye kholo la banja la Aarodi; Areli, ndiye kholo la banja la Aareli.