Numeri 26:17 - Buku Lopatulika17 Arodi, ndiye kholo la banja la Aarodi; Areli, ndiye kholo la banja la Aareli. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Arodi, ndiye kholo la banja la Aarodi; Areli, ndiye kholo la banja la Aareli. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Arodi anali kholo la banja la Aarodi. Areli anali kholo la banja la Aareli. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 kuchokera mwa Arodi, fuko la Aarodi; kuchokera mwa Arieli, fuko la a Areli. Onani mutuwo |