Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:13 - Buku Lopatulika

Zera, ndiye kholo la banja la Azera; Shaulo, ndiye kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zera, ndiye kholo la banja la Azera; Shaulo, ndiye kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zera anali kholo la banja la Azera. Shaulo anali kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuchokera mwa Zera, mbumba ya Zera; kuchokera mwa Sauli, fuko la Asauli.

Onani mutuwo



Numeri 26:13
6 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Simeoni: Yemuwele ndi Yamini, ndi Ohadi, ndi Yakini, ndi Zohari, ndi Shaulo, mwana wamwamuna wa mkazi wa ku Kanani.


Wachisanu ndi chitatu wa mwezi wachisanu ndi chitatu ndiye Sibekai Muhusa wa Azera; ndi m'chigawo mwake zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Wakhumi wa mwezi wakhumi ndiye Maharai Mnetofa wa Azera; ndi m'chigawo mwake zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Ana aamuna a Simeoni monga mwa mabanja ao ndiwo: Nemuwele, ndiye kholo la banja la Anemuwele; Yamini, ndiye kholo la banja la Ayamini; Yakini, ndiye kholo la banja la Ayakini;


Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana ziwiri.


nayandikizitsa zibale za Yuda, nagwira chibale cha Azera; nayandikizitsa chibale cha Azera, mmodzimmodzi, nagwidwa Zabidi;