Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:1 - Buku Lopatulika

Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Utatha mliriwo, Chauta adauza Mose ndi Eleazara, mwana wa wansembe Aroni, kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Utatha mliri Yehova anati kwa Mose ndi Eliezara mwana wa Aaroni,

Onani mutuwo



Numeri 26:1
3 Mawu Ofanana  

Monga Yehova analamula Mose, momwemo anawawerenga m'chipululu cha Sinai.


popeza akusautsani ndi manyengo ao amene anakunyengani nao; m'chija cha Peori, ndi cha Kozibi, mwana wamkazi wa kalonga wa ku Midiyani, mlongo wao, amene adamupha tsiku la mliri, m'chija cha Peori.


Ndipo akufa nao mliri ndiwo zikwi makumi awiri ndi zinai.