Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 22:2 - Buku Lopatulika

Ndipo Balaki mwana wa Zipori anaona zonse Israele anachitira Aamori.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Balaki mwana wa Zipori anaona zonse Israele anachitira Aamori.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Balaki mwana wa Zipora adaona zonse zimene Aisraele adachita Aamori.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Balaki mwana wa Zipori anaona zonse zimene Aisraeli anachitira Aamori,

Onani mutuwo



Numeri 22:2
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anamvera mau a Israele, napereka Akanani; ndipo anawaononga konse ndi mizinda yao yomwe; natcha dzina lake la malowo Horoma.


Pamenepo Balaki mwana wa Zipori, mfumu ya Mowabu, anauka naponyana ndi Israele; natuma naitana Balamu mwana wa Beori atemberere inu;


Ndipo tsopano kodi inu ndinu wabwino woposa Balaki mwana wa Zipori, mfumu ya Mowabu; anatengana konse ndi Israele iyeyu kodi, kapena kuchita nao nkhondo konse kodi?