Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 21:12 - Buku Lopatulika

Pochokapo anayenda ulendo, namanga mahema m'chigwa cha Zeredi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pochokapo anayenda ulendo, namanga mahema m'chigwa cha Zeredi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atachoka kumeneko, adakamanga m'chigwa cha Zeredi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kuchoka kumeneko anayendabe nakamanga misasa yawo mʼchigwa cha Zeredi.

Onani mutuwo



Numeri 21:12
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anachoka ku Oboti, namanga mahema ku Iyeabarimu, m'chipululu chakuno cha Mowabu, kotulukira dzuwa.


Nachokera ku Iyimu, nayenda namanga mu Diboni Gadi.


Uka, yenda ulendo wako, ndi kuoloka mtsinje wa Arinoni; taonani, ndapereka Sihoni mfumu ya Hesiboni, Mwamori, ndi dziko lake m'dzanja lako; yamba kulilandira, ndi kuutsana naye nkhondo.