Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 21:11 - Buku Lopatulika

Ndipo anachoka ku Oboti, namanga mahema ku Iyeabarimu, m'chipululu chakuno cha Mowabu, kotulukira dzuwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anachoka ku Oboti, namanga mahema ku Iyeabarimu, m'chipululu chakuno cha Mowabu, kotulukira dzuwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo adachoka ku Oboti nakamanga ku Iyeabarimu m'chipululu choyang'anana ndi Mowabu, kuvuma.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anasamuka ku Oboti nakamanga misasa yawo ku Iye-Abarimu, mʼchipululu chimene chili kummawa kwa Mowabu, kotulukira dzuwa.

Onani mutuwo



Numeri 21:11
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo ana a Israele anayenda ulendo, namanga mahema mu Oboti.


Pochokapo anayenda ulendo, namanga mahema m'chigwa cha Zeredi.


Nachokera ku Punoni, nayenda namanga mu Oboti.


Nachokera ku Oboti, nayenda namanga mu Iyeabarimu, m'malire a Mowabu.