Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 2:28 - Buku Lopatulika

Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo ankhondo ake ngokwanira 41,500.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 41,500.

Onani mutuwo



Numeri 2:28
4 Mawu Ofanana  

owerengedwa ao a fuko la Asere, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu.


Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Asere; ndi kalonga wa ana a Asere ndiye Pagiyele mwana wa Okarani.


Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.


Iwo ndiwo mabanja a ana aamuna a Asere monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.