Numeri 2:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Asere; ndi kalonga wa ana a Asere ndiye Pagiyele mwana wa Okarani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo iwo a kumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Asere; ndi kalonga wa ana a Asere ndiye Pagiyele mwana wa Okarani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Amene amange pafupi ndi fuko lake akhale a fuko la Asere, limene mtsogoleri wake ndi Pagiyele mwana wa Okarani, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Fuko la Aseri lidzamanga pafupi ndi iwowo. Mtsogoleri wa Aaseri ndi Pagieli mwana wa Okirani. Onani mutuwo |