Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:29 - Buku Lopatulika

29 Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Tsono pabwere fuko la Nafutali, limene mtsogoleri wake ndi Ahira mwana wa Enani,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Lotsatira lidzakhala fuko la Nafutali. Mtsogoleri wa Anafutali ndi Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:29
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Rakele anati, Ndi malimbano a Mulungu ndalimbana naye mkulu wanga, ndipo ndapambana naye; ndipo anamutcha dzina lake Nafutali.


Wa Nafutali, Ahira mwana wa Enani.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu.


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.


Tsiku lakhumi ndi chiwiri kalonga wa ana a Nafutali, ndiye Ahira mwana wa Enani:


ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ichi ndi chopereka cha Ahira mwana wa Enani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa