Numeri 2:29 - Buku Lopatulika29 Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Tsono pabwere fuko la Nafutali, limene mtsogoleri wake ndi Ahira mwana wa Enani, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Lotsatira lidzakhala fuko la Nafutali. Mtsogoleri wa Anafutali ndi Ahira mwana wa Enani. Onani mutuwo |