Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:41 - Buku Lopatulika

41 owerengedwa ao a fuko la Asere, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 owerengedwa ao a fuko la Asere, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Asere, adapezeka kuti ali 41,500.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Aseri chinali 41,500.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:41
4 Mawu Ofanana  

A ana a Asere, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


A ana a Nafutali, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu.


Iwo ndiwo mabanja a ana aamuna a Asere monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa