Numeri 1:41 - Buku Lopatulika41 owerengedwa ao a fuko la Asere, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 owerengedwa ao a fuko la Asere, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Asere, adapezeka kuti ali 41,500. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Aseri chinali 41,500. Onani mutuwo |