Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:47 - Buku Lopatulika

47 Iwo ndiwo mabanja a ana aamuna a Asere monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Iwo ndiwo mabanja a ana amuna a Asere monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 Ameneŵa, anthu okwanira 53,400, ndiwo adaŵerengedwa pa mabanja a Asere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Awa ndiwo anali mafuko a Aseri. Onse amene anawerengedwa analipo 53,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:47
3 Mawu Ofanana  

Ndipo dzina la mwana wamkazi wa Asere ndiye Sera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa