Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:46 - Buku Lopatulika

46 Ndipo dzina la mwana wamkazi wa Asere ndiye Sera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

46 Ndipo dzina la mwana wamkazi wa Asere ndiye Sera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

46 Mwana wamkazi wa Asere anali Sera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

46 (Aseri anali ndi mwana wamkazi dzina lake Sera)

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:46
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Asere: Imina, ndi Isiva, ndi Isivi, ndi Beriya, ndi Sera mlongo wao; ndi ana a Beriya: Hebere, ndi Malikiele.


Ana a Beriya ndiwo: Hebere, ndiye kholo la banja la Ahebere; Malikiele, ndiye kholo la banja la Amalikiele.


Iwo ndiwo mabanja a ana aamuna a Asere monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa