Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 2:21 - Buku Lopatulika

Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo ankhondo ake ngokwanira 32,200.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 32,200.

Onani mutuwo



Numeri 2:21
4 Mawu Ofanana  

owerengedwa ao a fuko la Manase, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana awiri.


Ndipo oyandikizana naye ndiwo a fuko la Manase; ndi kalonga wa ana a Manase ndiye Gamaliele mwana wa Pedazuri.


Ndi fuko la Benjamini: kalonga wa ana a Benjamini ndiye Abidani mwana wa Gideoni.


Iwo ndiwo mabanja ao a Manase; ndipo owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi asanu mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri.