Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 2:21 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 32,200.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

21 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 ndipo ankhondo ake ngokwanira 32,200.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:21
4 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Manase chinali 32,200.


Fuko la Manase lidzakhala pafupi ndi Efereimu. Mtsogoleri wa Amanase ndi Gamalieli mwana wa Pedazuri.


Lotsatira lidzakhala fuko la Benjamini. Mtsogoleri wa Abenjamini ndi Abidani mwana wa Gideoni.


Awa ndiwo anali mafuko a Manase. Amene anawerengedwa analipo 52,700.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa