Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 16:48 - Buku Lopatulika

Ndipo anaima pakati pa akufa ndi amoyo; ndi mliri unaleka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anaima pakati pa akufa ndi amoyo; ndi mliri unaleka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Aroni adakaima pakati pa anthu akufa ndi amoyo aja, ndipo mliriwo udaleka.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anayimirira pakati pa anthu amoyo ndi akufa ndipo mliri unaleka.

Onani mutuwo



Numeri 16:48
14 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anamangirapo Yehova guwa la nsembe, napereka nsembe zopsereza, ndi nsembe zoyamika. Momwemo Yehova anapembedzeka chifukwa cha dziko, ndi mliri wa pa Israele unalekeka.


Pamenepo panauka Finehasi, nachita chilango: Ndi mliriwo unaletseka.


Potero munthu yense anatenga mbale yake yofukizamo, naikamo moto, naikapo chofukiza, naima pa khomo la chihema chokomanako pamodzi ndi Mose ndi Aroni.


Ndipo moto unatuluka kwa Yehova, ndi kunyeketsa amuna mazana awiri ndi makumi asanu aja akubwera nacho chofukiza.


Ndipo Aroni anatenga monga Mose adanena, nathamanga kulowa pakati pa msonkhano; ndipo taonani, udayamba mliri pakati pa anthu; ndipo anaikapo chofukiza nawachitira anthu chowatetezera.


Koma akufa nao mliri ndiwo zikwi khumi ndi zinai mphambu mazana asanu ndi awiri, osawerenga aja adafera chija cha Kora.


Zitapita izi Yesu anampeza mu Kachisi, nati kwa iye, Taona, wachiritsidwa; usachimwenso, kuti chingakugwere choipa choposa.


ndi kulindirira Mwana wake achokere Kumwamba, amene anamuukitsa kwa akufa, Yesu, wotipulumutsa ife kumkwiyo ulinkudza.


Chifukwa chake muvomerezane wina ndi mnzake machimo anu, ndipo mupempherere wina kwa mnzake kuti muchiritsidwe. Pemphero la munthu wolungama likhoza kwakukulu m'machitidwe ake.