Numeri 16:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo moto unatuluka kwa Yehova, ndi kunyeketsa amuna mazana awiri ndi makumi asanu aja akubwera nacho chofukiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo moto unatuluka kwa Yehova, ndi kunyeketsa amuna mazana awiri ndi makumi asanu aja akubwera nacho chofukiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Tsono padayaka moto wochokera kwa Chauta ndipo udapsereza anthu 250 amene ankafukiza lubani aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Ndipo moto wochokera kwa Yehova unabwera nʼkunyeketsa anthu 250 amene ankapereka nsembe yofukiza aja. Onani mutuwo |