Numeri 16:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo Aisraele onse akukhala pozinga pao anathawa pakumva kufuula kwao; pakuti anati, Lingatimeze dziko ifenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo Aisraele onse akukhala pozinga pao anathawa pakumva kufuula kwao; pakuti anati, Lingatimeze dziko ifenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Pomwepo Aisraele onse amene anali pafupi adathaŵa, atamva anthuwo akulira. Ankati, “Tiyeni tithaŵe kuti nthakayi ingatimeze nafenso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Atamva kulira kwawo, Aisraeli onse amene anali pafupi ndi anthuwo anathawa akufuwula kuti, “Nthaka imezanso ife!” Onani mutuwo |