2 Samueli 24:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo Davide anamangirapo Yehova guwa la nsembe, napereka nsembe zopsereza, ndi nsembe zoyamika. Momwemo Yehova anapembedzeka chifukwa cha dziko, ndi mliri wa pa Israele unalekeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo Davide anamangirapo Yehova guwa la nsembe, napereka nsembe zopsereza, ndi nsembe zoyamika. Momwemo Yehova anapembedzeka chifukwa cha dziko, ndi mliri wa pa Israele unalekeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Ndipo kumeneko adamangako guwa, kumangira Chauta, napereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano. Choncho Chauta adamva kupemba kwake kopembera dziko, ndipo mliriwo udaleka m'dziko la Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Davide anamanga guwa lansembe la Yehova pamenepo ndipo anaperekapo nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano. Ndipo Yehova anayankha pempherolo mʼmalo mwa dziko lonse, ndipo mliri unatha pa Aisraeli. Onani mutuwo |