1 Mafumu 1:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo mfumu Davide anakalamba nachuluka masiku ake; ndipo iwo anamfunda ndi zofunda, koma iye sanafundidwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo mfumu Davide anakalamba nachuluka masiku ake; ndipo iwo anamfunda ndi zofunda, koma iye sanafundidwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mfumu Davide anali wokalamba kwambiri. Ndipo ngakhale ankamufunditsa mabulangete, sankamvabe kufunda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mfumu Davide atakalamba sankamva kufunda ngakhale akamufunditsa mabulangeti. Onani mutuwo |