Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 11:7 - Buku Lopatulika

Ndipo mana ananga zipatso zampasa, ndi maonekedwe ake ngati maonekedwe a bedola.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mana ananga zipatso zampasa, ndi maonekedwe ake ngati maonekedwe a bedola.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Manayo ankafanafana ndi njere za mapira, ndipo maonekedwe ake anali ngati ulimbo wouma.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mana ankafanana ndi mbewu zamapira ndipo maonekedwe ake anali ngati ulimbo wowuma.

Onani mutuwo



Numeri 11:7
7 Mawu Ofanana  

golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.


Ndipo ananena nao, Ichi ndi chomwe Yehova analankhula, Mawa ndiko kupuma, Sabata lopatulika la Yehova; chimene muziotcha, otchani, ndi chimene muziphika phikani; ndi chotsala chikukhalireni chosungika kufikira m'mawa.


Ndipo mbumba ya Israele inautcha dzina lake Mana; ndiwo ngati zipatso zampasa, oyera; powalawa akunga timitanda tosakaniza ndi uchi.


Anthu amanka, nawaola, nawapera ndi mphero, kapena kuwasinja mumtondo, nawaphika m'mphika, nawaumba timitanda; ndi powalawa anali ngati timitanda tokazinga ndi mafuta.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wopambana, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pamwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu aliyense koma iye wakuulandira.