Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 11:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Mana ankafanana ndi mbewu zamapira ndipo maonekedwe ake anali ngati ulimbo wowuma.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

7 Ndipo mana ananga zipatso zampasa, ndi maonekedwe ake ngati maonekedwe a bedola.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo mana ananga zipatso zampasa, ndi maonekedwe ake ngati maonekedwe a bedola.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Manayo ankafanafana ndi njere za mapira, ndipo maonekedwe ake anali ngati ulimbo wouma.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 11:7
7 Mawu Ofanana  

(Golide wa ku dziko ili ndi wabwino. Kulinso miyala yokongola ya bedola ndi onikisi).


Iye anawawuza kuti, “Izi ndi zimene Yehova analamula, ‘Mawa ndi tsiku lopumula, Sabata Loyera la Yehova, choncho wotchani ndi kuphika zimene mukufuna. Sungani zotsala mpaka mmawa.’ ”


Aisraeli anatchula chakudyacho Mana. Chakudyacho chinkaoneka ngati mbewu zamapira, zoyera. Ndipo chinkakoma ngati chothira uchi.


Anthu ankapita kukatola manawo, nʼkumasinja mu mtondo kapena kupera. Ankawaphika mu mʼphika kapena kupanga makeke. Ndipo ankakoma ngati makeke ophikira mafuta a olivi.


Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo. Kwa amene adzapambane ndidzamupatsa chakudya chobisika cha mana. Ndidzamupatsanso mwala woyera wolembedwapo dzina latsopano, lodziwa iye yekha amene walandirayo.’ ”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa