Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 11:14 - Buku Lopatulika

Sinditha kuwasenza anthu awa onse ndekha, pakuti andilemera ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Sinditha kuwasenza anthu awa onse ndekha, pakuti andilemera ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ine sindingathe kuŵasamala ndekha anthu onseŵa. Katundu ameneyu sindingathe kumsenza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Sindingathe kusamala anthu onsewa ndekha. Katundu ameneyu ndi wolemera kwambiri kwa ine.

Onani mutuwo



Numeri 11:14
6 Mawu Ofanana  

Pamenepo munalankhula m'masomphenya ndi okondedwa anu, ndipo mudati, Ndasenza thandizo pa chiphona; ndakweza wina wosankhika mwa anthu.


Udzalema konse, iwe ndi anthu amene uli nao; pakuti chikukanika chinthu ichi; sungathe kuchichita pa wekha.


Pakuti kwa ife mwana wakhanda wabadwa, kwa ife mwana wamwamuna wapatsidwa; ndipo ulamuliro udzakhala pa phewa lake, ndipo adzamutcha dzina lake Wodabwitsa, Wauphungu, Mulungu wamphamvu, Atate Wosatha, Kalonga wa mtendere.


inde adzamanga Kachisi wa Yehova; nadzasenza ulemererowo, nadzakhala ndi kulamulira pa mpando wachifumu wake; nadzakhala wansembe pampando wachifumu wake; ndi uphungu wa mtendere udzakhala pakati pa iwo awiri.


koma kwa ena fungo la moyo kumoyo. Ndipo azikwanira ndani izi?