Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 18:18 - Buku Lopatulika

18 Udzalema konse, iwe ndi anthu amene uli nao; pakuti chikukanika chinthu ichi; sungathe kuchichita pa wekha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Udzalema konse, iwe ndi anthu amene uli nao; pakuti chikukanika chinthu ichi; sungathe kuchichita pa wekha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Inu mudzafooka msanga, pamodzi ndi anthu muli nawoŵa. Ntchito imeneyi njaikulu kuposa mphamvu zanu, ndipo simungaithe nokha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ntchitoyi ndi yayikulu kuposa mphamvu zanu. Inu simungathe kuyigwira nokha. Inu pamodzi ndi anthuwa amene amabwera kwa inu mudzatopa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 18:18
7 Mawu Ofanana  

Koma mpongozi wa Mose ananena naye, Chinthu uchitachi sichili chabwino ai.


Ndipo ndidzapereka ndi kuperekedwa konse chifukwa cha miyoyo yanu mokondweratu. Ngati ndikonda inu kochuluka koposa, kodi ndikondedwa kochepa?


pakuti chifukwa cha ntchito ya Khristu anafikira pafupi imfa, wosasamalira moyo wake, kuti akakwaniritse chiperewero cha utumiki wanu wa kwa ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa