Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:6 - Buku Lopatulika

Mukalizanso chokweza, a m'zigono za kumwera ayende; alize chokweza pakumuka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mukalizanso chokweza, a m'zigono za kumwera ayende; alize chokweza pakumuka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mukaliza lipenga lochenjeza kachiŵiri, anthu a m'mahema akumwera ayambepo ulendo. Muziŵalizira lipenga lochenjezalo nthaŵi zonse akamanyamuka ulendo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Akaliza lipenga lochenjeza lachiwiri, misasa yakummwera iyambe kusamuka. Kuliza kwa lipenga lochenjeza kudzakhala chizindikiro choyamba ulendo.

Onani mutuwo



Numeri 10:6
3 Mawu Ofanana  

Ndi a mbendera ya chigono cha Rubeni, anayenda monga mwa magulu ao; ndipo pa gulu lake anayang'anira Elizuri mwana wa Sedeuri.


Pomemeza msonkhano mulize, wosati chokweza ai.