Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:5 - Buku Lopatulika

Mukaliza chokweza ayende a m'zigono za kum'mawa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mukaliza chokweza ayende a m'zigono za kum'mawa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mukaliza lipenga lochenjeza, anthu a m'mahema akuvuma ayambepo ulendo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Akaliza lipenga lochenjeza, misasa yomwe ili kummawa iyambe kusamuka.

Onani mutuwo



Numeri 10:5
5 Mawu Ofanana  

Fuula zolimba, usalekerere, kweza mau ako ngati lipenga, ndi kuwafotokozera anthu anga cholakwa chao, ndi banja la Yakobo machimo ao.


Muombe lipenga mu Ziyoni, nimufuulitse m'phiri langa lopatulika; onse okhala m'dziko anjenjemere; pakuti tsiku la Yehova lilinkudza, pakuti liyandikira;


Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.