Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:3 - Buku Lopatulika

Akaliza, khamu lonse lisonkhane kuli iwe ku khomo la chihema chokomanako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akaliza, khamu lonse lisonkhane kuli iwe ku khomo la chihema chokomanako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akaliza aŵiri onsewo, mpingo wonse usonkhane kwa iwe pa chipata cha chihema chamsonkhano.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene akuliza malipenga onse awiri, anthu onse asonkhane kwa iwe pa khomo la tenti ya msonkhano.

Onani mutuwo



Numeri 10:3
3 Mawu Ofanana  

Nenani mu Yuda, lalikirani mu Yerusalemu, ndi kuti, Ombani lipenga m'dzikomo; fuulani, ndi kuti, Sonkhanani pamodzi, tilowe m'mizinda ya malinga.


Muombe lipenga mu Ziyoni, nimufuulitse m'phiri langa lopatulika; onse okhala m'dziko anjenjemere; pakuti tsiku la Yehova lilinkudza, pakuti liyandikira;