Yeremiya 4:5 - Buku Lopatulika5 Nenani mu Yuda, lalikirani mu Yerusalemu, ndi kuti, Ombani lipenga m'dzikomo; fuulani, ndi kuti, Sonkhanani pamodzi, tilowe m'mizinda ya malinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Nenani m'Yuda, lalikirani m'Yerusalemu, ndi kuti, Ombani lipenga m'dzikomo; fuulani, ndi kuti, Sonkhanani pamodzi, tilowe m'midzi ya malinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Lalika ku Yuda, lengeza ku Yerusalemu kuti, “Lizani lipenga m'dziko lonse, ndi kufuula kuti, ‘Sonkhanani, tiyeni tipite ku mizinda ku Ziyoni.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Lengeza ku Yuda ndi kulalikira mu Yerusalemu kuti, ‘Lizani lipenga mʼdziko lonse!’ Ndipo fuwulani kuti, ‘Sonkhanani! Tiyeni tithawire ku mizinda yotetezedwa!’ Onani mutuwo |