Yeremiya 4:4 - Buku Lopatulika4 Mudzidulire nokha kwa Yehova, chotsani khungu la mitima yanu, amuna inu a Yuda ndi okhala mu Yerusalemu; ukali wanga ungatuluke ngati moto, ungatenthe kuti sangathe kuuzima, chifukwa cha kuipa kwa machitidwe anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mudzidulire nokha kwa Yehova, chotsani khungu la mitima yanu, amuna inu a Yuda ndi okhala m'Yerusalemu; ukali wanga ungatuluke ngati moto, ungatenthe kuti sangathe kuuzima, chifukwa cha kuipa kwa machitidwe anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Muzikhala okhulupirika ndi kumanditumikira Ine Chauta ndi mtima wanu wonse. Muzichita zimenezi inu anthu a ku Yuda ndi inu okhala ku Yerusalemu, kuwopa kuti mkwiyo wanga ungabuke ngati moto, ndi kukuyakirani chifukwa cha ntchito zanu zoipa, osapezeka wina aliyense wotha kuuzimitsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Dziperekeni nokha kwa Ine kuti munditumikire ndi mtima wanu wonse, inu anthu a ku Yuda ndi ku Yerusalemu. Muzichita zimenezi kuopa kuti mkwiyo wanga ungabuke ngati moto ndi kukutenthani, chifukwa cha ntchito zanu zoyipazo popanda wina wowuzimitsa. Onani mutuwo |