Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:20 - Buku Lopatulika

Ndi pa gulu la fuko la ana a Gadi anayang'anira Eliyasafu mwana wa Deuwele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pa gulu la fuko la ana a Gadi anayang'anira Eliyasafu mwana wa Deuwele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtsogoleri wa gulu la fuko la Agadi anali Eliyasafu mwana wa Deuwele.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo Eliyasafu mwana wa Deuweli ndiye ankatsogolera fuko la Gadi.

Onani mutuwo



Numeri 10:20
5 Mawu Ofanana  

Wa Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Simeoni anayang'anira Selumiele mwana wa Zurishadai.


Pamenepo Akohati anayenda, ndi kunyamula zopatulika, ndi enawo anautsiratu chihema asanafike iwowa.


Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele.


Tsiku lachisanu ndi chimodzi kalonga wa ana a Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele: