Numeri 10:21 - Buku Lopatulika21 Pamenepo Akohati anayenda, ndi kunyamula zopatulika, ndi enawo anautsiratu chihema asanafike iwowa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pamenepo Akohati anayenda, ndi kunyamula zopatulika, ndi enawo anautsiratu Kachisi asanafike iwowa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Tsono Akohati atasenza zinthu zopatulika, adanyamuka. Malo opatulika anali atamangidwiratu iwowo asanafike. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kenaka Akohati ananyamuka atanyamula zinthu zopatulika. Chihema chinkayenera kuyimikidwa iwo asanafike. Onani mutuwo |