Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:19 - Buku Lopatulika

Ndi pa gulu la fuko la ana a Simeoni anayang'anira Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pa gulu la fuko la ana a Simeoni anayang'anira Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtsogoleri wa gulu la Asimeoni anali Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mtsogoleri wa fuko la Simeoni anali Selumieli mwana wa Zurisadai,

Onani mutuwo



Numeri 10:19
4 Mawu Ofanana  

Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.


Ndi a mbendera ya chigono cha Rubeni, anayenda monga mwa magulu ao; ndipo pa gulu lake anayang'anira Elizuri mwana wa Sedeuri.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Gadi anayang'anira Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Tsiku lachisanu kalonga wa ana a Simeoni, ndiye Selumiele, mwana wa Zurishadai: