Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:36 - Buku Lopatulika

36 Tsiku lachisanu kalonga wa ana a Simeoni, ndiye Selumiele, mwana wa Zurishadai:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Tsiku lachisanu kalonga wa ana a Simeoni, ndiye Selumiele, mwana wa Zurishadai:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Tsiku lachisanu linali la Selumiele mwana wa Zurishadai, mtsogoleri wa Asimeoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Pa tsiku lachisanu Selumieli mwana wa Zurisadai, mtsogoleri wa fuko la Simeoni, anabweretsa chopereka chake.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:36
4 Mawu Ofanana  

Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.


Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Simeoni; ndi kalonga wa ana a Simeoni ndiye Selumiele mwana wa Zurishadai.


ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Elizuri mwana wa Sedeuri.


chopereka chake ndicho mbale imodzi yasiliva, kulemera kwake masekeli zana limodzi ndi makumi atatu, mbale yowazira imodzi yasiliva ya masekeli makumi asanu ndi awiri, kuyesa sekeli wa malo opatulika; zonse ziwiri zodzala ndi ufa wosakaniza ndi mafuta, ukhale nsembe yaufa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa