Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:8 - Buku Lopatulika

Wa Isakara, Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa Isakara, Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

fuko la Isakara, Netanele mwana wa Zuwara;

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Netanieli mwana wa Zuwara, kuchokera ku fuko la Isakara,

Onani mutuwo



Numeri 1:8
5 Mawu Ofanana  

Wa Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu.


Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Isakara panali Netanele mwana wa Zuwara.


Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Isakara; ndipo kalonga wa ana a Isakara ndiye Netanele mwana wa Zuwara.


Tsiku lachiwiri Netanele mwana wa Zuwara, kalonga wa Isakara, anabwera nacho chake: