Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 10:15 - Buku Lopatulika

15 Ndi pa gulu la fuko la ana a Isakara panali Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndi pa gulu la fuko la ana a Isakara panali Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Mtsogoleri wa gulu la fuko la Isakara anali Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mtsogoleri wa gulu la fuko la Isakara anali Netanieli mwana wa Zuwara,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:15
4 Mawu Ofanana  

Wa Isakara, Netanele mwana wa Zuwara.


Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndi gulu la fuko la ana a Zebuloni panali Eliyabu mwana wa Heloni.


Tsiku lachiwiri Netanele mwana wa Zuwara, kalonga wa Isakara, anabwera nacho chake:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa