Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:15 - Buku Lopatulika

Wa Nafutali, Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa Nafutali, Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

fuko la Nafutali, Ahira mwana wa Enani.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ahira mwana wa Enani, kuchokera ku fuko la Nafutali.”

Onani mutuwo



Numeri 1:15
5 Mawu Ofanana  

Wa Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Iwo ndiwo oitanidwa a khamu, akalonga a mafuko a makolo ao; ndiwo akulu a zikwizo za Israele.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.


Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.


Tsiku lakhumi ndi chiwiri kalonga wa ana a Nafutali, ndiye Ahira mwana wa Enani: