Wa Nafutali, Ahira mwana wa Enani.
fuko la Nafutali, Ahira mwana wa Enani.”
Ahira mwana wa Enani, kuchokera ku fuko la Nafutali.”
Wa Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele.
Iwo ndiwo oitanidwa a khamu, akalonga a mafuko a makolo ao; ndiwo akulu a zikwizo za Israele.
Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.
Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.
Tsiku lakhumi ndi chiwiri kalonga wa ana a Nafutali, ndiye Ahira mwana wa Enani: