Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 10:3 - Buku Lopatulika

Pasuri, Amariya, Malikiya,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pasuri, Amariya, Malikiya,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pasuri, Amariya, Malakiya,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pasuri, Amariya, Malikiya,

Onani mutuwo



Nehemiya 10:3
13 Mawu Ofanana  

mwana wa Mikaele, mwana wa Baaseiya, mwana wa Malikiya,


ndi Adaya mwana wa Yerohamu, mwana wa Pasuri, mwana wa Malikiya, ndi Maasai mwana wa Adiyele, mwana wa Yazera, mwana wa Mesulamu, mwana wa Mesilemiti, mwana wa Imeri,


Seraya, Azariya, Yeremiya,


Hatusi, Sebaniya, Maluki,


Seraya mwana wa Hilikiya, mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki, mwana wa Meraiyoti, mwana wa Ahitubi mtsogoleri wa m'nyumba ya Mulungu;


ndi abale ao ochita ntchito ya m'nyumbayi ndiwo mazana asanu ndi atatu mphambu makumi awiri kudza awiri; ndi Adaya mwana wa Yerohamu, mwana wa Pelaliya, mwana wa Amizi, mwana wa Zekariya, mwana wa Pasuri, mwana wa Malikiya;


Ndipo ansembe ndi Alevi amene anakwera ndi Zerubabele mwana wa Sealatiele, ndi Yesuwa, ndi awa: Seraya, Yeremiya, Ezara,


wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanani;


Amariya, Maluki, Hatusi,


ndi Azariya, Ezara ndi Mesulamu,


Yuda, ndi Benjamini, ndi Semaya, ndi Yeremiya,


Malikiya mwana wa Harimu, ndi Hasubu mwana wa Pahatimowabu, anakonza gawo lina, ndi Nsanja ya Ng'anjo.


Ndipo Ezara mlembi anaima pa chiunda cha mitengo adachimangira msonkhanowo; ndi pambali pake padaima Matitiya, ndi Sema, ndi Anaya, ndi Uriya, ndi Hilikiya, ndi Maaseiya, kudzanja lamanja lake; ndi kudzanja lamanzere Pedaya, ndi Misaele, ndi Malikiya, ndi Hasumu, ndi Hasibadana, Zekariya, ndi Mesulamu.