Nehemiya 12:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo ansembe ndi Alevi amene anakwera ndi Zerubabele mwana wa Sealatiele, ndi Yesuwa, ndi awa: Seraya, Yeremiya, Ezara, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ansembe ndi Alevi amene anakwera ndi Zerubabele mwana wa Sealatiele, ndi Yesuwa, ndi awa: Seraya, Yeremiya, Ezara, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ansembe ndi Alevi, amene adabwerera pamodzi ndi Zerubabele mwana wa Sealatiele, ndiponso ndi Yesuwa, anali aŵa: Seraya, Yeremiya, Ezara, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ansembe ndi Alevi amene anabwerera pamodzi ndi Zerubabeli mwana wa Sealatieli ndi Yesuwa anali awa: Seraya, Yeremiya, Ezara, Onani mutuwo |
Chaka chachiwiri tsono chakufika iwo kunyumba ya Mulungu ku Yerusalemu, mwezi wachiwiri, Zerubabele mwana wa Sealatiele, ndi Yesuwa mwana wa Yozadaki, ndi abale ao otsala, ansembe ndi Alevi, ndi onse ochokera kundende kudza ku Yerusalemu, anayamba, naika Alevi a zaka makumi awiri ndi mphambu, ayang'anire ntchito ya nyumba ya Yehova.