Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 10:2 - Buku Lopatulika

2 Seraya, Azariya, Yeremiya,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Seraya, Azariya, Yeremiya,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Senaya, Azariya, Yeremiya,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Seraya, Azariya, Yeremiya

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 10:2
7 Mawu Ofanana  

Ndipo kazembe anawauza kuti asadyeko zopatulika kwambiri, mpaka adzabuka wansembe wokhala ndi Urimu ndi Tumimu.


Okhomera chizindikiro tsono ndiwo Nehemiya, Tirisata mwana wa Hakaliya, ndi Zedekiya,


Pasuri, Amariya, Malikiya,


Seraya mwana wa Hilikiya, mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki, mwana wa Meraiyoti, mwana wa Ahitubi mtsogoleri wa m'nyumba ya Mulungu;


Ndipo ansembe ndi Alevi amene anakwera ndi Zerubabele mwana wa Sealatiele, ndi Yesuwa, ndi awa: Seraya, Yeremiya, Ezara,


Potsatizana nao anakonza Benjamini ndi Hasubu pandunji pa nyumba pao. Potsatizana nao anakonza Azariya mwana wa Maaseiya mwana wa Ananiya pafupi pa nyumba yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa