Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 5:41 - Buku Lopatulika

Ndipo amene akakukakamiza kumperekeza njira imodzi, upite naye ziwiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo amene akakukakamiza kumperekeza njira imodzi, upite naye ziwiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu akakukakamiza kuyenda naye mtunda umodzi, uyende naye mitunda iŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati wina akukakamiza kuti uyende naye mtunda umodzi, iwe uyende naye mitunda iwiri.

Onani mutuwo



Mateyu 5:41
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pakutuluka pao anapeza munthu wa ku Kirene, dzina lake Simoni, namkakamiza iye kuti anyamule mtanda wake.


Ndipo kwa iye wofuna kupita nawe kumlandu ndi kutenga malaya ako, umlolezenso chofunda chako.


Kwa iye wopempha iwe umpatse, ndipo kwa iye wofuna kukukongola usampotolokere.


Ndipo anakakamiza wina wopitirirapo, Simoni wa ku Kirene, alikuchokera kuminda, atate wao wa Aleksandro ndi Rufu, kuti anyamule mtanda wake.


Ndipo popita naye, anagwira munthu, Simoni wa ku Kirene, alikuchokera kuminda, namsenza iye mtanda aunyamule pambuyo pake pa Yesu.


Pakuti chikondi cha Khristu chitikakamiza; popeza taweruza chotero, kuti mmodzi adafera onse, chifukwa chake onse adafa;