Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 5:2 - Buku Lopatulika

ndipo anatsegula pakamwa, nawaphunzitsa iwo, nati:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo anatsegula pakamwa, nawaphunzitsa iwo, nati:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kenaka adayamba kuŵaphunzitsa, adati,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo anayamba kuwaphunzitsa kuti,

Onani mutuwo



Mateyu 5:2
11 Mawu Ofanana  

Atatero, Yobu anatsegula pakamwa pake, natemberera tsiku lake.


imvani, pakuti ndikanena zoposa, ndi zolungama potsegula pakamwa panga.


kuti chikachitidwe chonenedwa ndi mneneri, kuti, Ndidzatsegula pakamwa panga ndi mafanizo; ndidzawulula zinthu zobisika chiyambire kukhazikidwa kwake kwa dziko lapansi.


Ndipo m'mene Iye anaona makamu, anakwera m'phiri; ndipo m'mene Iye anakhala pansi, anadza kwa Iye ophunzira ake;


Ndipo Petro anatsegula pakamwa pake, nati, Zoona ndizindikira kuti Mulungu alibe tsankho;


Koma pamene Paulo anati atsegule pakamwa pake, Galio anati kwa Ayuda, Ukadakhala mlandu wa chosalungama, kapena dumbo loipa, Ayuda inu, mwenzi nditakumverani inu;


Ndipo Filipo anatsegula pakamwa pake, nayamba pa lembo ili, nalalikira kwa iye Yesu.


ndi ine ndemwe, kuti andipatse mau m'kunditsegulira m'kamwa molimbika, kuti ndizindikiritse anthu chinsinsicho cha Uthenga Wabwino,