Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 3:1 - Buku Lopatulika

1 Atatero, Yobu anatsegula pakamwa pake, natemberera tsiku lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Atatero, Yobu anatsegula pakamwa pake, natemberera tsiku lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Pambuyo pake Yobe adalankhula, nayamba kutemberera tsiku lake lobadwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Pambuyo pake Yobu anatsekula pakamwa pake nayamba kutemberera tsiku limene iyeyo anabadwa.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 3:1
12 Mawu Ofanana  

Koma mutambasule dzanja lanu ndi kumkhudzira zake zonse, ndipo adzakuchitirani mwano pamaso panu.


Mwa ichi chonse Yobu sanachimwe, kapena kunenera Mulungu cholakwa.


Nakhala pansi pamodzi naye panthaka masiku asanu ndi awiri usana ndi usiku, palibe mmodzi ananena naye kanthu, popeza anaona kuti kuwawaku nkwakukulu ndithu.


Koma tambasulani dzanja lanu, ndi kukhudza fupa lake ndi mnofu wake, ndipo adzakuchitirani mwano pamaso panu.


Nalankhula Yobu nati,


Litayike tsiku lobadwa ine, ndi usikuwo udati, Waima naye mwana wamwamuna.


chifukwa chake Yobu anatsegula pakamwa pake mwachabe, nachulukitsa mau opanda nzeru.


Pakuti anawawitsa mzimu wake, ndipo analankhula zosayenera ndi milomo yake.


Kalanga ine, amai, pakuti mwandibala ine munthu wandeu, munthu wakutetana nalo dziko lonse lapansi! Sindinakongoletsa paphindu, anthu sanandikongoletse paphindu; koma iwo onse anditemberera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa