Machitidwe a Atumwi 10:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo Petro anatsegula pakamwa pake, nati, Zoona ndizindikira kuti Mulungu alibe tsankho; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo Petro anatsegula pakamwa pake, nati, Zoona ndizindikira kuti Mulungu alibe tsankho; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Petro adayamba kulankhula, adati, “Zoonadi ndazindikira tsopano kuti Mulungu alibe tsankho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Ndipo Petro anayamba kuyankhula nati, “Zoonadi, tsopano ndazindikira kuti Mulungu sakondera. Onani mutuwo |