Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:6 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene Yesu anali mu Betaniya, m'nyumba ya Simoni wakhate,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene Yesu anali m'Betaniya, m'nyumba ya Simoni wakhate,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsiku lina Yesu anali ku Betaniya, m'nyumba ya Simoni wotchedwa Wakhate.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu ali ku Betaniya mʼnyumba Simoni Wakhate,

Onani mutuwo



Mateyu 26:6
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anawasiya, natuluka m'mzinda, napita ku Betaniya, nagona kumeneko.


Ndipo m'mawa mwake, atatuluka ku Betaniya, Iye anamva njala.