Ndipo pamene Yesu anali mu Betaniya, m'nyumba ya Simoni wakhate,
Ndipo pamene Yesu anali m'Betaniya, m'nyumba ya Simoni wakhate,
Tsiku lina Yesu anali ku Betaniya, m'nyumba ya Simoni wotchedwa Wakhate.
Yesu ali ku Betaniya mʼnyumba Simoni Wakhate,
Ndipo Iye anawasiya, natuluka m'mzinda, napita ku Betaniya, nagona kumeneko.
Ndipo m'mawa mwake, atatuluka ku Betaniya, Iye anamva njala.