Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 21:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo Iye anawasiya, natuluka m'mzinda, napita ku Betaniya, nagona kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Iye anawasiya, natuluka m'mzinda, napita ku Betaniya, nagona kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Pamenepo Yesu adaŵasiya, natuluka mumzindamo kupita ku Betaniya, nakagona kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ndipo anawasiya natuluka mu mzindawo ndi kupita ku Betaniya, kumene anakagona.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 21:17
16 Mawu Ofanana  

Ulangizidwe, Yerusalemu, ungakuchokere moyo wanga, ndingakuyese iwe bwinja, dziko losakhalamo anthu.


Angakhale alera ana ao, koma ndidzawasowetsa, wosatsala munthu; ndithunso tsoka iwowa, pamene ndiwachokera.


Obadwa oipa ndi achigololo afunafuna chizindikiro; ndipo sadzalandira chizindikiro china, koma chizindikiro cha Yona. Ndipo Iye anawasiya, nachokapo.


Ndipo pamene Yesu anali mu Betaniya, m'nyumba ya Simoni wakhate,


Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, ku Betefage ndi Betaniya, paphiri la Azitona, anatuma awiri a ophunzira ake,


Ndipo Iye analowa mu Yerusalemu, mu Kachisi; ndipo m'mene anaunguza zinthu zonse, popeza ndi madzulo, anatuluka kupita ku Betaniya pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.


Ndipo masiku onse madzulo anatuluka Iye m'mzinda.


Ndipo pakukhala Iye ku Betaniya m'nyumba ya Simoni wakhate, m'mene anaseama kudya, anadzapo mkazi ali nayo nsupa ya alabastero ya mafuta onunkhira bwino a narido weniweni a mtengo wapatali; naswa nsupayo, nawatsanulira pamutu pake.


Ndipo Yesu anachokako pamodzi ndi ophunzira ake nanka kunyanja: ndipo linamtsata khamu lalikulu la a ku Galileya, ndi a ku Yudeya,


Ndipo pakupita paulendo pao Iye analowa m'mudzi wina; ndipo mkazi wina dzina lake Marita anamlandira Iye kunyumba kwake.


Ndipo kunali, m'mene anayandikira ku Betefage ndi Betaniya, paphiri lotchedwa la Azitona, anatuma awiri a ophunzira,


Ndipo anatuluka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ake, nawadalitsa.


Koma panali munthu wodwala, Lazaro wa ku Betaniya, wa m'mudzi wa Maria ndi mbale wake Marita.


Koma Betaniya anali pafupi pa Yerusalemu, nthawi yake yonga ya mastadiya khumi ndi asanu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa