Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:44 - Buku Lopatulika

Ndipo anawasiyanso, napemphera kachitatu, nateronso mau omwewo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anawasiyanso, napemphera kachitatu, nateronso mau omwewo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adaŵasiyanso, napita kukapemphera kachitatu, akunena mau amodzimodzi omwe aja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho anawasiya napitanso kukapemphera kachitatu nanenanso chimodzimodzi.

Onani mutuwo



Mateyu 26:44
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anabweranso, nawapeza iwo ali m'tulo, pakuti zikope zao zinalemera ndi tulo.


Pomwepo anadza kwa ophunzira, nanena kwa iwo, Gonani nthawi yatsalayi, mupumule; onani, nthawi yafika, ndipo Mwana wa Munthu aperekedwa m'manja a ochimwa.


Ndipo popemphera musabwerezebwereze chabe iai, monga amachita anthu akunja, chifukwa ayesa kuti adzamvedwa ndi kulankhulalankhula kwao.


Ndipo anawanenera fanizo lakuti ayenera iwo kupemphera nthawi zonse, osafooka mtima;


Za ichi ndinapemphera Ambuye katatu kuti chichoke kwa ine.